akondakitale - gwamba lyrics
[intro: lawi]
yi, aye*iye*yah
aye*iye*yah
[chorus: lawi]
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
inu ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi
[verse 1:gwamba]
aish, ndalama nde yavuta pa nyasa
daily fans k*mayisaka
sikuwona zoti ndiwe shasha
k*menya business basi k*mayitsatsa
nde mukapeza ka ndalama sister, chonde k*makagwiritsitsa
mukamagona nako kukafunditsa
kwachuluka mbava nde muzikabisa
[chorus: lawi]
yi, ndikupempha mundithandize
yi, w*ngondivuta ndi uphawi (ayi)
ah, ah
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
inu ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi
[verse 2: gwamba]
aish, conductor pokwera umati 100 ndangokhala pansi ukuti 120
aseh, osaziyamba zin*z*
muno sindichoka ngati sundipatsa change
wekha ukudziwa dollar ili pa minga
povaya kudedza pena kukwera njinga
umayesa ngati ukundiyimba
lero lonkha wandilira sindiyimva
[chorus: lawi]
yi, ndikupempha mundithandize
yi, w*ngondivuta ndi uphawi (ayi)
ah, ah
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
inu ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi
[verse 3: gwamba]
aish, komanso yesu akufuna change mama
koma change akufuna iye si ndalama
akufunitsitsa inuyo makamaka mutasintha ndikuyamba k*mutsata
mapemphero ndi hustle ya uzimu
mukapusa tsiku lomaliza, no change
mapemphero ndi hustle ya uzimu
ukapusa tsiku lomaliza, no change
[chorus: lawi]
yi, ndikupempha mundithandize
yi, w*ngondivuta ndi umphawi
ah, ah
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko change
inu ulendo w*nga ukathera ku lilongwe, m’deport
koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi
Random Song Lyrics :
- slowmo - rizha lyrics
- parlé - sal houdini lyrics
- honest - jae young lyrics
- for you - seinabo sey lyrics
- insolação - vinícius viana lyrics
- ready (feat. ramon revere) - art morera lyrics
- rad - why nkkné lyrics
- baddlan de kaalje - amrinder gill lyrics
- just beyond your smile - the sunshine company lyrics
- grow wings - dbo (korea) lyrics